Masalimo 136:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo anapereka dziko lao likhale cholowa; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo anapereka dziko lao likhale chosiyira; pakuti chifundo chake nchosatha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Napereka dziko la mafumuwo kuti likhale choloŵa, pakuti chikondi chake nchamuyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Napereka dziko lawo ngati cholowa, pakuti chikondi chake chosasinthika nʼchamuyaya. Onani mutuwo |