Masalimo 130:7 - Buku Lopatulika7 Israele, uyembekezere Yehova; chifukwa kwa Yehova kuli chifundo, kwaonso kuchulukira chiombolo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Israele, uyembekezere Yehova; chifukwa kwa Yehova kuli chifundo, kwaonso kuchulukira chiombolo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Iwe Israele, khulupirira Chauta. Paja Chauta ndi wa chikondi chosasinthika, ndi wokonzeka kupulumutsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Yembekeza Yehova, iwe Israeli, pakuti Yehova ali ndi chikondi chosasinthika ndipo alinso ndi chipulumutso chochuluka. Onani mutuwo |