Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 129:8 - Buku Lopatulika

8 Angakhale opitirirapo sanena, Dalitso la Mulungu likhale pa inu; tikudalitsani m'dzina la Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Angakhale opitirirapo sanena, Dalitso la Mulungu likhale pa inu; tikudalitsani m'dzina la Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Anthu odutsapo sadzanena kwa omwetawo kuti, “Madalitso a Chauta akhale nanu.” “Tikukudalitsani potchula dzina la Chauta.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Odutsa pafupi asanene kuti, “Dalitso la Yehova lili pa inu; tikukudalitsani mʼdzina la Yehova.”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 129:8
3 Mawu Ofanana  

Pamene Davide adatsiriza kupereka nsembe yopsereza ndi zoyamika, iye anawadalitsa anthuwo m'dzina la Yehova wa makamu.


Wodala wakudzayo m'dzina la Yehova; takudalitsani kochokera m'nyumba ya Yehova.


Ndipo taona, Bowazi anafuma ku Betelehemu, nati kwa ocheka, Yehova akhale nanu. Namyankha iwo, Yehova akudalitseni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa