Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 129:7 - Buku Lopatulika

7 umene womweta sadzaza nao dzanja lake, kapena womanga mitolo sakupatira manja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 umene womweta sadzaza nao dzanja lake, kapena womanga mitolo sakupatira manja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Woumweta sangadzaze nkumanja komwe, womanga mitolo sangamange nchitsakato chomwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 sungadzaze manja a owumweta kapena manja a omanga mitolo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 129:7
4 Mawu Ofanana  

Iye amene ayendayenda nalira, ponyamula mbeu yakufesa; adzabweranso ndithu ndi kufuula mokondwera, alikunyamula mitolo yake.


Pakuti abzala mphepo, nadzakolola kamvulumvulu; alibe tirigu wosasenga; ngala siidzatulutsa ufa; chinkana iutulutsa, alendo adzaumeza.


Pakuti wakufesera kwa thupi la iye yekha, chochokera m'thupi adzatuta chivundi; koma wakufesera kwa Mzimu, chochokera mu Mzimu adzatuta moyo wosatha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa