Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 129:6 - Buku Lopatulika

6 Akhale ngati udzu womera patsindwi, wakufota asanauzule;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Akhale ngati udzu womera patsindwi, wakufota asanauzule;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba, umene umafota usanakule.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba, umene umafota usanakule;

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 129:6
7 Mawu Ofanana  

ndipo, taona, ngala zisanu ndi ziwiri zina zofota, zoonda, zopserera ndi mphepo ya kum'mawa, zinamera pambuyo pao;


Chifukwa chake okhalamo ao anali ofooka manja, anaopsedwa, nachita manyazi, ananga udzu wakuthengo, ndi msipu wauwisi, ndi udzu wa patsindwi, ndi tirigu wopserera asanakule.


Pakuti adzawamweta msanga monga udzu, ndipo adzafota monga msipu wauwisi.


chakuti pophuka oipa ngati msipu, ndi popindula ochita zopanda pake; chitero kuti adzaonongeke kosatha.


Chifukwa chake okhalamo analefuka, naopsedwa, nathedwa nzeru; ananga udzu wa m'munda, ndi masamba awisi, ndi udzu wa pamatsindwi, ndi munda wa tirigu asanakule.


Ndipo m'mene dzuwa linakwera zinapserera; ndipo popeza zinalibe mizu zinafota.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa