Masalimo 129:5 - Buku Lopatulika5 Achite manyazi nabwerere m'mbuyo. Onse akudana naye Ziyoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Achite manyazi nabwerere m'mbuyo. Onse akudana naye Ziyoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Anthu onse odana ndi Ziyoni agonjetsedwe ndi kupirikitsidwa mwamanyazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Onse amene amadana ndi Ziyoni abwezedwe pambuyo mwamanyazi. Onani mutuwo |
Ndipo kudzafanana ndi munthu wanjala, pamene alota, ndipo, taonani, akudya; koma auka, ndipo m'kati mwake muli zii; kapena monga munthu waludzu pamene alota, ndipo taonani, akumwa; koma auka ndipo taonani walefuka, ndipo m'kati mwake muli gwaa; momwemo lidzakhala khamu la mitundu yonse yomenyana ndi phiri la Ziyoni.