Masalimo 126:4 - Buku Lopatulika4 Bwezani ukapolo wathu, Yehova, ngati mitsinje ya kumwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Bwezani ukapolo wathu, Yehova, ngati mitsinje ya kumwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tibwezereni ufulu wathu, Inu Chauta, tikhale ngati mitsinje yam'chipululu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova, monga mitsinje ya ku Negevi. Onani mutuwo |