Masalimo 126:1 - Buku Lopatulika1 Pobweza Yehova ukapolo wa Ziyoni, tinakhala ngati anthu akulota. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Pobweza Yehova ukapolo wa Ziyoni, tinakhala ngati anthu akulota. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamene Chauta adabwezera akapolo ku Ziyoni, tinali ngati anthu amene akulota. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni, tinali ngati amene akulota. Onani mutuwo |