Masalimo 125:5 - Buku Lopatulika5 Koma iwo akupatula kutsata njira zao zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi ochita zopanda pake. Mtendere ukhale pa Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Koma iwo akupatula kutsata njira zao zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi ochita zopanda pake. Mtendere ukhale pa Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Koma anthu amene amatsata njira zao zokhotakhota, Chauta adzaŵapirikitsira kumene kuli anthu ochita zoipa. Mtendere ukhale ndi Israele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa. Mtendere ukhale pa Israeli. Onani mutuwo |