Masalimo 124:7 - Buku Lopatulika7 Moyo wathu unaonjoka ngati mbalame mu msampha wa msodzi; msampha unathyoka ndi ife tinaonjoka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Moyo wathu unaonjoka ngati mbalame mu msampha wa msodzi; msampha unathyoka ndi ife tinaonjoka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Taonjoka ngati mbalame mu msampha wa osaka, msampha wathyoka, ndipo ife tapulumuka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Moyo wathu wawonjoka ngati mbalame yokodwa mu msampha wa mlenje; msampha wathyoka, ndipo ife tapulumuka. Onani mutuwo |