Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 124:6 - Buku Lopatulika

6 Alemekezedwe Yehova, amene sanatipereke kumano kwao tikhale chakudya chao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Alemekezedwe Yehova, amene sanatipereke kumano kwao tikhale chakudya chao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Atamandike Chauta, amene sadatipereke kwa anthuwo kuti atiwononge.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Atamandike Yehova, amene sanalole kuti tikhale chakudya cha mano awo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 124:6
7 Mawu Ofanana  

Kundikankha anandikankha ndikadagwa; koma Yehova anandithandiza.


kundilanditsa kwa oipa amene andipasula, adani a pa moyo wanga amene andizinga.


Chifukwa chake tsono, mwazi wanga usagwe pansi kutali ndi Yehova; pakuti mfumu ya Israele yatuluka kudzafuna nsabwe, monga munthu wosaka nkhwali pamapiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa