Masalimo 119:99 - Buku Lopatulika99 Ndili nayo nzeru yakuposa aphunzitsi anga onse; pakuti ndilingalira mboni zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201499 Ndili nayo nzeru yakuposa aphunzitsi anga onse; pakuti ndilingalira mboni zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa99 Ndili ndi nzeru za kumvetsa kupambana aphunzitsi anga onse, pakuti ndimasinkhasinkha za malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero99 Ndimamvetsa zinthu kwambiri kuposa aphunzitsi anga onse popeza ndimalingalira umboni wanu. Onani mutuwo |