Masalimo 119:98 - Buku Lopatulika98 Malamulo anu andipatsa nzeru yakuposa adani anga; pakuti akhala nane chikhalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201498 Malamulo anu andipatsa nzeru yakuposa adani anga; pakuti akhala nane chikhalire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa98 Malamulo anu amandisandutsa wanzeru kuposa adani anga, popeza kuti malamulowo ndili nawo nthaŵi zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero98 Malamulo anu amachititsa kuti ndikhale wanzeru kuposa adani anga, popeza malamulowo ali ndi ine nthawi zonse. Onani mutuwo |