Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:97 - Buku Lopatulika

97 Ha! Ndikondadi chilamulo chanu; ndilingiriramo ine tsiku lonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

97 Ha! Ndikondadi chilamulo chanu; ndilingiriramo ine tsiku lonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

97 Ndimakonda malamulo anu kwambiri, ndimasinkhasinkha za malamulowo tsiku lonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

97 Ndithu, ine ndimakonda malamulo anu! Ndimalingaliramo tsiku lonse.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:97
14 Mawu Ofanana  

Komatu m'chilamulo cha Yehova muli chikondwerero chake; ndipo m'chilamulo chake amalingirira usana ndi usiku.


Ndidana nao a mitima iwiri; koma ndikonda chilamulo chanu.


Chifukwa chake ndikonda malamulo anu koposa golide, inde golide woyengeka.


Ndidzalingirira pa malangizo anu, ndi kupenyerera mayendedwe anu.


Penyani kuti ndikonda malangizo anu; mundipatse moyo, Yehova, monga mwa chifundo chanu.


Akukonda chilamulo chanu ali nao mtendere wambiri; ndipo alibe chokhumudwitsa.


Moyo wanga unasamalira mboni zanu; ndipo ndizikonda kwambiri.


Ndipo ndidzadzikondweretsa nao malamulo anu, amene ndiwakonda.


Ndidzakwezanso manja anga ku malamulo anu, amene ndiwakonda; ndipo ndidzalingalira pa malemba anu.


Wopanduka afunafuna chifuniro chake, nakangana ndi nzeru yonse yeniyeni.


Pakuti nzeru idzalowa m'mtima mwako, moyo wako udzakondwera ndi kudziwa,


ndipo azikhala nacho, nawerengemo masiku onse a moyo wake; kuti aphunzire kuopa Yehova Mulungu wake, kusunga mau onse a chilamulo ichi ndi malemba awa, kuwachita;


Buku ili la chilamulo lisachoke pakamwa pako; koma ulingiriremo usana ndi usiku, kuti usamalire kuchita monga mwa zonse zolembedwamo; popeza ukatero udzakometsa njira yako, nudzachita mwanzeru.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa