Masalimo 119:96 - Buku Lopatulika96 Ndinapenya malekezero ake a ungwiro wonse; koma lamulo lanu ndi lotakasuka ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201496 Ndinapenya malekezero ake a ungwiro wonse; koma lamulo lanu ndi lotakasuka ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa96 Ndazindikira kuti zabwino zonse zili ndi malire, koma malamulo anu alibe konse malire. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero96 Ndadziwa kuti zinthu zonse zili ndi malire, koma malamulo anu alibe malire konse. Onani mutuwo |