Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:94 - Buku Lopatulika

94 Ine ndine wanu, ndipulumutseni pakuti ndinafuna malangizo anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

94 Ine ndine wanu, ndipulumutseni pakuti ndinafuna malangizo anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

94 Ndine wanu, pulumutseni, pakuti ndasamala malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

94 Ndine wanu, ndipulumutseni; pakuti ndasamala malangizo anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:94
17 Mawu Ofanana  

Ndinaitanira Inu; ndipulumutseni, ndipo ndidzasamalira mboni zanu.


Kupemba kwanga kudze pamaso panu; mundilanditse monga mwa mau anu.


Dzanja lanu likhale lakundithandiza; popeza ndinasankha malangizo anu.


Mundizindikiritse njira ya malangizo anu; kuti ndilingalire zodabwitsa zanu.


Taonani, ndinalira malangizo anu; mundipatse moyo mwa chilungamo chanu.


Ndipo ndidzayenda mwaufulu; popeza ndinafuna malangizo anu.


Chipulumutso ncha Yehova; dalitso lanu likhale pa anthu anu.


Sungani moyo wanga pakuti ine ndine wokondedwa wanu; Inu Mulungu wanga, pulumutsani mtumiki wanu wokhulupirira Inu.


Ndine wake wa wokondedwa wanga, wokondedwa wanganso ndiye wa ine; aweta zake pakati pa akakombo.


atero Yehova, amene anakutenga iwe, nakuumba kuchokera m'mimba, amene adzathangata iwe. Usaope Yakobo, mtumiki wanga ndi iwe, Yesuruni, amene ndakusankha iwe.


Wina adzati, Ine ndili wa Yehova; ndi wina adzadzitcha yekha ndi dzina la Yakobo, ndipo wina adzalemba ndi dzanja lake, Ndine wa Yehova, ndi kudzitcha yekha ndi mfunda wa Israele.


Mundichiritse ine, Yehova, ndipo ndidzachiritsidwa; mundipulumutse ine, ndipo ndidzapulumutsidwa; pakuti chilemekezo changa ndinu.


Yehova Mulungu wako ali pakati pako, wamphamvu wakupulumutsa; adzakondwera nawe ndi chimwemwe, adzakhala wopanda thamo m'chikondi chake; adzasekerera nawe ndi kuimbirapo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa