Masalimo 119:94 - Buku Lopatulika94 Ine ndine wanu, ndipulumutseni pakuti ndinafuna malangizo anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201494 Ine ndine wanu, ndipulumutseni pakuti ndinafuna malangizo anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa94 Ndine wanu, pulumutseni, pakuti ndasamala malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero94 Ndine wanu, ndipulumutseni; pakuti ndasamala malangizo anu. Onani mutuwo |