Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:93 - Buku Lopatulika

93 Sindidzaiwala malangizo anu nthawi zonse; popeza munandipatsa nao moyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

93 Sindidzaiwala malangizo anu nthawi zonse; popeza munandipatsa nao moyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

93 Sindidzaiŵala konse malangizo anu, pakuti mwandipatsa nawo moyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

93 Ine sindidzayiwala konse malangizo anu, pakuti ndi malangizo anuwo munasunga moyo wanga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:93
5 Mawu Ofanana  

Ndidzadzikondweretsa nao malemba anu; sindidzaiwala mau anu.


Moyo wanga umamatika ndi fumbi; mundipatse moyo monga mwa mau anu.


Chitonthozo changa m'kuzunzika kwanga ndi ichi; pakuti mau anu anandipatsa moyo.


Wopatsa moyo ndi mzimu; thupi silithandiza konse. Mau amene ndalankhula ndi inu ndiwo mzimu, ndi moyo.


inu amene mudabadwanso, osati ndi mbeu yofeka, komatu yosaola, mwa mau a Mulungu amoyo ndi okhalitsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa