Masalimo 119:91 - Buku Lopatulika91 Kunena za maweruzo anu alimbikira kufikira lero; pakuti onsewa ndiwo atumiki anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201491 Kunena za maweruzo anu alimbikira kufikira lero; pakuti onsewa ndiwo atumiki anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa91 Zolengedwa zikupezeka lero lino chifukwa cha kulamula kwanu, pakuti zinthu zonse zimakutumikirani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero91 Malamulo anu alipobe mpaka lero lino, pakuti zinthu zonse zimatumikira Inu. Onani mutuwo |