Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:89 - Buku Lopatulika

89 Mau anu aikika kumwamba, kosatha, Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

89 Mau anu aikika kumwamba, kosatha, Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

89 Inu Chauta, mau anu ngokhazikika kumwambako mpaka muyaya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

89 Mawu anu Yehova ndi amuyaya; akhazikika kumwambako.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:89
10 Mawu Ofanana  

Ntchito za manja ake ndizo choonadi ndi chiweruzo; malangizo ake onse ndiwo okhulupirika.


Achirikizika kunthawi za nthawi, achitika m'choonadi ndi chilunjiko.


Kuyambira kale ndinadziwa mu mboni zanu, kuti munazikhazika kosatha.


Chiwerengero cha mau anu ndicho choonadi; ndi maweruzo anu olungama onse akhala kosatha.


Pakuti ndinati, Chifundo adzachimanga kosaleka; mudzakhazika chikhulupiriko chanu mu Mwamba mwenimweni.


Udzu unyala, duwa lifota, koma mau a Mulungu wathu adzakhala nthawi zachikhalire.


Pakuti indetu ndinena kwa inu, Kufikira litapitirira thambo ndi dziko, kalemba kakang'ono kamodzi kapena kansonga kake kamodzi sikadzachokera kuchilamulo, kufikira zitachitidwa zonse.


koma Mau a Ambuye akhala chikhalire. Ndipo mau olalikidwa kwa inu ndi awo.


Koma monga mwa lonjezano lake tiyembekezera miyamba yatsopano, ndi dziko latsopano m'menemo mukhalitsa chilungamo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa