Masalimo 119:88 - Buku Lopatulika88 Mundipatse moyo monga mwa chifundo chanu; ndipo ndidzasamalira mboni ya pakamwa panu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201488 Mundipatse moyo monga mwa chifundo chanu; ndipo ndidzasamalira mboni ya pakamwa panu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa88 Sungani moyo wanga chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika, kuti nditsate malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero88 Sungani moyo wanga molingana ndi chikondi chanu chosasinthika, ndipo ndidzamvera umboni wa pakamwa panu. Onani mutuwo |