Masalimo 119:85 - Buku Lopatulika85 Odzikuza anandikumbira mbuna, ndiwo osasamalira chilamulo chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201485 Odzikuza anandikumbira mbuna, ndiwo osasamalira chilamulo chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa85 Anthu osasamala za Mulungu, osatsata malamulo anu, andikumbira mbuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero85 Anthu osalabadira za Mulungu, odzikuza amandikumbira dzenje motsutsana ndi malamulo anu. Onani mutuwo |