Masalimo 119:81 - Buku Lopatulika81 Moyo wanga unakomoka ndi kukhumba chipulumutso chanu: Ndinayembekezera mau anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201481 Moyo wanga unakomoka ndi kukhumba chipulumutso chanu: Ndinayembekezera mau anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa81 Moyo wanga wafooka podikira chipulumutso chanu, ndikukhulupirira mau anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero81 Moyo wanga wafowoka ndi kufunafuna chipulumutso chanu, koma chiyembekezo changa chili mʼmawu anu. Onani mutuwo |