Masalimo 119:80 - Buku Lopatulika80 Mtima wanga ukhale wangwiro m'malemba anu; kuti ndisachite manyazi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201480 Mtima wanga ukhale wangwiro m'malemba anu; kuti ndisachite manyazi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa80 Mtima wanga ukhale wopanda choudzudzulira pa malamulo anu, kuti ndisachite manyazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero80 Mtima wanga ukhale wopanda cholakwa pa chiphunzitso chanu kuti ndisachititsidwe manyazi. Onani mutuwo |