Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:74 - Buku Lopatulika

74 Iwo amene akuopani adzandiona ine nadzakondwera; popeza ndayembekezera mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

74 Iwo amene akuopani adzandiona ine nadzakondwera; popeza ndayembekezera mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

74 Anthu okuwopani adzandiwona ndipo adzakondwa, popeza kuti ndakhulupirira mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

74 Iwo amene amakuopani akondwere akandiona, chifukwa chiyembekezo changa chili mʼmawu anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:74
10 Mawu Ofanana  

Mulungu analankhula m'chiyero chake; ndidzakondwerera: ndidzagawa Sekemu; ndidzayesa muyeso chigwa cha Sukoti.


Ndinafuula kusanake: ndinayembekezera mau anu.


Kuti ndikhale nao mau akuyankha wonditonza; popeza ndikhulupirira mau anu.


Ndipo musandichotsere ndithu mau a choonadi pakamwa panga; pakuti ndinayembekeza maweruzo anu.


Iwo akuopa Inu abwere kwa ine, ndipo adzadziwa mboni zanu.


Idzani, imvani, inu nonse akuopa Mulungu, ndipo ndidzafotokozera zonse anazichitira moyo wanga.


Pamenepo iwo akuopa Yehova analankhulana wina ndi mnzake; ndipo Yehova anawatchera khutu namva, ndi buku la chikumbutso linalembedwa pamaso pake, la kwa iwo akuopa Yehova, nakumbukira dzina lake.


Thambo ndi dziko lapansi zidzapita; koma mau anga sadzapita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa