Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:71 - Buku Lopatulika

71 Kundikomera kuti ndinazunzidwa; kuti ndiphunzire malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

71 Kundikomera kuti ndinazunzidwa; kuti ndiphunzire malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

71 Ndi bwino kuti ndidalangidwa, kuti ndiphunzire malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

71 Ndi bwino kuti ndinasautsidwa kuti ndithe kuphunzira malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:71
5 Mawu Ofanana  

Ndisanazunzidwe ndinasokera; koma tsopano ndisamalira mau anu.


Chifukwa chake, mwa ichi choipa cha Yakobo chidzafafanizidwa, ndipo ichi ndi chipatso chonse chakuchotsa tchimo lake; pamene iye adzayesa miyala yonse ya guwa la nsembe, ngati miyala yanjeresa yoswekasweka, zifanizo ndi mafano a dzuwa sizidzaukanso konse.


Koma poweruzidwa, tilangidwa ndi Ambuye, kuti tingatsutsidwe pamodzi ndi dziko lapansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa