Masalimo 119:70 - Buku Lopatulika70 Mtima wao unona ngati mafuta; koma ine ndikondwera nacho chilamulo chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201470 Mtima wao unona ngati mafuta; koma ine ndikondwera nacho chilamulo chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa70 Anthu otere ndi opulukira, koma ine ndimakondwa ndi malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero70 Mitima yawo ndi yowuma ndi yosakhudzidwa, koma ine ndimakondwera ndi malamulo anu. Onani mutuwo |