Masalimo 119:68 - Buku Lopatulika68 Inu ndinu wabwino, ndi wakuchita zabwino; mundiphunzitse malemba anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201468 Inu ndinu wabwino, ndi wakuchita zabwino; mundiphunzitse malemba anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa68 Inu ndinu abwino, ndipo mumachita zabwino, phunzitseni malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero68 Inu ndinu abwino ndipo zimene mumachita ndi zabwino; phunzitseni malamulo anu. Onani mutuwo |