Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:68 - Buku Lopatulika

68 Inu ndinu wabwino, ndi wakuchita zabwino; mundiphunzitse malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

68 Inu ndinu wabwino, ndi wakuchita zabwino; mundiphunzitse malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

68 Inu ndinu abwino, ndipo mumachita zabwino, phunzitseni malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

68 Inu ndinu abwino ndipo zimene mumachita ndi zabwino; phunzitseni malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:68
14 Mawu Ofanana  

Aleluya. Yamikani Yehova; pakuti Iye ndiye wabwino: Pakuti chifundo chake nchosatha.


Yamikani Yehova pakuti Iye ndiye wabwino; pakuti chifundo chake nchosatha.


Inu ndinu wodala Yehova; ndiphunzitseni malemba anu.


Ndinafotokozera njira zanga, ndipo munandiyankha: Mundiphunzitse malemba anu.


Pakuti Inu, Ambuye, ndinu wabwino, ndi wokhululukira, ndi wa chifundo chochulukira onse akuitana Inu.


Ndidzatchula zachifundo chake cha Yehova, ndi matamando a Yehova, monga mwa zonse zimene Yehova wapereka kwa ife; ndi ubwino wake waukulu kwa banja la Israele, umene Iye wapereka kwa iwo, monga mwa chifundo chake, ndi monga mwa ntchito zochuluka za chikondi chake.


Ndipo Iye anati kwa iye, Undifunsiranji za chinthu chabwino? Alipo Mmodzi ndiye wabwino: koma ngati ufuna kulowa m'moyo, sunga malamulo.


kotero kuti mukakhale ana a Atate wanu wa Kumwamba; chifukwa Iye amakwezera dzuwa lake pa oipa ndi pa abwino, namavumbitsira mvula pa olungama ndi pa osalungama.


Ndipo Yesu anati kwa iye, Unditcha Ine wabwino bwanji? Palibe wabwino koma mmodzi, ndiye Mulungu.


Koma Yesu anati kwa iye, Unditcha Ine wabwino bwanji? Palibe wabwino, koma mmodzi, ndiye Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa