Masalimo 119:61 - Buku Lopatulika61 Anandikulunga nazo zingwe za oipa; koma sindinaiwale chilamulo chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201461 Anandikulunga nazo zingwe za oipa; koma sindinaiwala chilamulo chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa61 Ngakhale anthu oipa anditchere msampha, sindiiŵala malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero61 Ngakhale oyipa andimange ndi zingwe, sindidzayiwala lamulo lanu. Onani mutuwo |