Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:57 - Buku Lopatulika

57 Yehova ndiye gawo langa: Ndinati ndidzasunga mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

57 Yehova ndiye gawo langa: Ndinati ndidzasunga mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

57 Inu Chauta, zanga zonse ndinu, ndikulonjeza kumvera mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

57 Yehova, Inu ndiye gawo langa; ndalonjeza kumvera mawu anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:57
16 Mawu Ofanana  

Ndinalumbira, ndipo ndinatsimikiza mtima, kuti ndidzasamalira maweruzo anu olungama.


Mundichokere ochita zoipa inu; kuti ndisunge malamulo a Mulungu wanga.


Odala iwo akusunga mboni zake, akumfuna ndi mtima wonse;


Ndinafuulira kwa inu, Yehova; ndinati, Inu ndinu pothawirapo panga, gawo langa m'dziko la amoyo.


Yehova ndiye gawo la cholowa changa ndi chikho changa, ndinu wondigwirira cholandira changa.


zimene inazitchula milomo yanga, ndinazinena pakamwa panga posautsika ine.


Likatha thupi langa ndi mtima wanga, Mulungu ndiye thanthwe la mtima wanga, ndi cholandira changa chosatha.


Gawo la Yakobo silifanana ndi iwo; pakuti Iye ndiye analenga zonse; Israele ndiye mtundu wa cholowa chake; dzina lake ndi Yehova wa makamu.


Moyo wanga uti, Gawo langa ndiye Yehova; chifukwa chake ndidzakhulupirira.


Alibe cholowa pakati pa abale ao; Yehova mwini wake ndiye cholowa chao, monga ananena nao.


Ndipo ngati kutumikira Yehova kukuipirani mudzisankhire lero amene mudzamtumikira, kapena milungu imene anaitumikira makolo anu okhala tsidya lija la mtsinje, kapena milungu ya Aamori amene mukhala m'dziko lao; koma ine, ndi a m'nyumba yanga, tidzatumikira Yehova.


ndipo Yehova anaingitsa pamaso pathu anthu awa onse, ngakhale Aamori okhala m'dzikomo; chifukwa chake ifenso tidzatumikira Yehova, pakuti ndiye Mulungu wathu.


Ndipo anthu anati kwa Yoswa, Iaitu, koma tidzatumikira Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa