Masalimo 119:54 - Buku Lopatulika54 Malemba anu anakhala nyimbo zanga m'nyumba ya ulendo wanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201454 Malemba anu anakhala nyimbo zanga m'nyumba ya ulendo wanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa54 Malamulo anu asanduka nyimbo yanga kulikonse kumene ndimapita. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero54 Zophunzitsa zanu ndi mitu ya nyimbo yanga kulikonse kumene ndigonako. Onani mutuwo |