Masalimo 119:53 - Buku Lopatulika53 Ndinasumwa kwakukulu, chifukwa cha oipa akusiya chilamulo chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201453 Ndinasumwa kwakukulu, chifukwa cha oipa akusiya chilamulo chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa53 Ndimapsa mtima kwambiri chifukwa cha anthu oipa amene amaphwanya malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero53 Ndayipidwa kwambiri chifukwa cha oyipa amene ataya malamulo anu. Onani mutuwo |