Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:52 - Buku Lopatulika

52 Ndinakumbukira maweruzo anu kuyambira kale, Yehova, ndipo ndinadzitonthoza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

52 Ndinakumbukira maweruzo anu kuyambira kale, Yehova, ndipo ndinadzitonthoza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

52 Inu Chauta, ndikamalingalira malamulo anu akalekale, ndimasangalala,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

52 Ndimakumbukira malamulo anu Yehova akalekale, ndipo mwa iwo ndimapeza chitonthozo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:52
10 Mawu Ofanana  

kwa iwo akusunga chipangano chake, ndi kwa iwo akukumbukira malangizo ake kuwachita.


Kumbukirani zodabwitsa zake adazichita; zizindikiro zake ndi maweruzo a pakamwa pake;


Ndikumbukira masiku a kale lomwe; zija mudazichita ndilingirirapo; ndikamba pandekha za ntchito ya manja anu.


Ndinaganizira masiku akale, zaka zakalekale.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa