Masalimo 119:51 - Buku Lopatulika51 Odzikuza anandinyoza kwambiri: koma sindinapatukanso nacho chilamulo chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201451 Odzikuza anandinyoza kwambiri: koma sindinapatukanso nacho chilamulo chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa51 Anthu osasamala za Mulungu amandinyoza kwathunthu, komabe sindisiyana nawo malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero51 Odzikuza amandinyoza popanda chowaletsa, koma sindichoka pa malamulo anu. Onani mutuwo |