Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:44 - Buku Lopatulika

44 Potero ndidzasamalira malamulo anu chisamalire kunthawi za nthawi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 Potero ndidzasamalira malamulo anu chisamalire kunthawi za nthawi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 Ndidzatsata malamulo anu kosalekeza mpaka muyaya,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 Ndidzasunga malamulo anu nthawi zonse, ku nthawi za nthawi.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:44
5 Mawu Ofanana  

Ndinalingitsa mtima wanga uchite malemba anu, kosatha, kufikira chimaliziro.


Usiku ndinakumbukira dzina lanu, Yehova, ndipo ndinasamalira chilamulo chanu.


Iye wakukhala wosalungama achitebe zosalungama; ndi munthu wonyansa akhalebe wonyansa; ndi iye wakukhala wolungama achitebe cholungama; ndi iye amene ali woyera akhalebe woyeretsedwa.


Chifukwa chake ali kumpando wachifumu wa Mulungu; ndipo amtumikira Iye usana ndi usiku mu Kachisi mwake; ndipo Iye wakukhala pa mpando wachifumu adzawachitira mthunzi,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa