Masalimo 119:34 - Buku Lopatulika34 Mundizindikiritse, ndipo ndidzasunga malamulo anu; ndidzawasamalira ndi mtima wanga wonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Mundizindikiritse, ndipo ndidzasunga malamulo anu; ndidzawasamalira ndi mtima wanga wonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Patseni nzeru kuti ndizisunga malamulo anu, ndiziŵatsata ndi mtima wanga wonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Mundipatse mtima womvetsa zinthu ndipo ndidzasunga malamulo anu ndi kuwamvera ndi mtima wanga wonse. Onani mutuwo |