Masalimo 119:25 - Buku Lopatulika25 Moyo wanga umamatika ndi fumbi; mundipatse moyo monga mwa mau anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Moyo wanga umamatika ndi fumbi; mundipatse moyo monga mwa mau anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Ndangoti thapsa m'fumbi. Bwezereni moyo monga momwe mudalonjezera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Moyo wanga wakangamira fumbi; tsitsimutseni molingana ndi mawu anu. Onani mutuwo |