Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:23 - Buku Lopatulika

23 Nduna zomwe zinakhala zondineneza; koma mtumiki wanu analingirira malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Nduna zomwe zinakhala zondineneza; koma mtumiki wanu analingirira malemba anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Ngakhale mafumu andichitire upo woipa, ine mtumiki wanu ndidzasinkhasinkhabe za malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Ngakhale mafumu akhale pamodzi kundinyoza, mtumiki wanu adzalingalirabe zophunzitsa zanu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:23
8 Mawu Ofanana  

Ndidzalingirira pa malangizo anu, ndi kupenyerera mayendedwe anu.


Nduna zinandilondola kopanda chifukwa; koma mtima wanga uchita nao mantha mau anu.


Ndipo pamene kunacha, bungwe la akulu a anthu linasonkhana, ndiwo ansembe aakulu ndi alembi; ndipo anapita naye kubwalo lao,


Popeza nthawi yonse mwana wa Yeseyo akhala ndi moyo padziko, koma sudzakhazikika iwe, kapena ufumu wako. Chifukwa chake tumiza tsopano numtengere kuno kwa ine, popeza adzafa ndithu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa