Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:22 - Buku Lopatulika

22 Mundichotsere chotonza, ndi chimpepulo; pakuti ndinasunga mboni zanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

22 Mundichotsere chotonza, ndi chimpepulo; pakuti ndinasunga mboni zanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

22 Mundichotsere zonyoza zao zondinyodola, chifukwa ndasunga malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

22 Mundichotsere chitonzo ndi mnyozo pakuti ndimasunga malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:22
18 Mawu Ofanana  

Mabwenzi anga andinyoza; koma diso langa lilirira misozi kwa Mulungu.


Mundipatutsire chotonza changa ndichiopacho; popeza maweruzo anu ndi okoma.


Kuti ndikhale nao mau akuyankha wonditonza; popeza ndikhulupirira mau anu.


Khulupirira Yehova, ndipo chita chokoma; khala m'dziko, ndipo tsata choonadi.


Ndipo adzaonetsa chilungamo chako monga kuunika, ndi kuweruza kwako monga usana.


Ndipulumutseni kwa zolakwa zanga zonse, musandiike ndikhale chotonza cha wopusa.


Adani anga andinyoza ndi kundithyola mafupa anga; pakunena ndine dzuwa lonse, Mulungu wako ali kuti?


Chifukwa chake titulukire kwa Iye kunja kwa tsasa osenza tonzo lake.


Pakuti mbiri yokoma yanji, mukapirira pochimwa ndi kubwanyulidwapo? Komatu, ngati pochita zabwino, ndi kumvako ndiko chisomo pa Mulungu.


Koma Nabala anayankha anyamata a Davide nati, Davide ndani? Ndi mwana wa Yese ndani? Masiku ano pali anyamata ambiri akungotaya ambuye ao.


Ndipo pamene Davide anamva kuti Nabala adamwalira, iye anati, Alemekezedwe Yehova, amene anaweruza mlandu wa mtonzo wanga wochokera ku dzanja la Nabala, naletsa mnyamata wake pa choipa; ndipo Yehova anabwezera pamutu pa Nabala choipa chake. Ndipo Davide anatumiza wokamfunsira Abigaile, zakuti amtengere akhale mkazi wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa