Masalimo 119:18 - Buku Lopatulika18 Munditsegulire maso, kuti ndipenye zodabwitsa za m'chilamulo chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Munditsegulire maso, kuti ndipenye zodabwitsa za m'chilamulo chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Tsekulani maso anga kuti ndiwone zodabwitsa zochokera m'malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Tsekulani maso anga kuti ndithe kuona zinthu zodabwitsa mʼmalamulo anu. Onani mutuwo |