Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:18 - Buku Lopatulika

18 Munditsegulire maso, kuti ndipenye zodabwitsa za m'chilamulo chanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Munditsegulire maso, kuti ndipenye zodabwitsa za m'chilamulo chanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Tsekulani maso anga kuti ndiwone zodabwitsa zochokera m'malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Tsekulani maso anga kuti ndithe kuona zinthu zodabwitsa mʼmalamulo anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:18
17 Mawu Ofanana  

Ndinapenya malekezero ake a ungwiro wonse; koma lamulo lanu ndi lotakasuka ndithu.


Ndipo tsiku limenelo gonthi adzamva mau a m'buku, ndi maso akhungu adzaona potuluka m'zoziya ndi mumdima.


Ndipo maso a iwo amene aona sadzatsinzina, ndi makutu a iwo amene amva adzamvera.


Pamenepo maso a akhungu adzatsegudwa, ndi makutu a ogontha adzatsegulidwa.


Ndinamlembera zinthu zambirimbirizo za chilamulo changa, koma zinayesedwa ngati chinthu chachilendo.


Chifukwa chake ndiphiphiritsira iwo m'mafanizo; chifukwa kuti akuona samaona, ndi akumva samamva, kapena samadziwitsa.


Ndipo Yesu anayankha iye, nati, Ndiwe wodala, Simoni Bara-Yona: pakuti thupi ndi mwazi sizinakuululire ichi, koma Atate wanga wa Kumwamba.


Ananena kwa Iye, Ambuye, kuti maso athu apenye.


Ndipo Yesu anati, Kudzaweruza ndadza Ine kudziko lino lapansi, kuti iwo osapenya apenye; ndi kuti iwo akupenya akhale osaona.


kukawatsegulira maso ao, kuti atembenuke kuchokera kumdima, kulinga kukuunika, ndi kuchokera ulamuliro wa Satana kulinga kwa Mulungu, kuti alandire iwo chikhululukiro cha machimo, ndi cholowa mwa iwo akuyeretsedwa ndi chikhulupiriro cha mwa Ine.


Pakuti chilamulo, pokhala nao mthunzi wa zokoma zilinkudza, osati chifaniziro chenicheni cha zinthuzo, sichikhozatu, ndi nsembe zomwezi chaka ndi chaka, zimene azipereka kosalekeza, kuwayesera angwiro iwo akuyandikira.


amene atumikira chifaniziro ndi mthunzi wa zakumwambazo monga Mose achenjezedwa m'mene anafuna kupanga chihema: pakuti, Chenjera, ati, uchite zonse monga mwa chitsanzocho chaonetsedwa kwa iwe m'phiri.


ndikulangiza ugule kwa Ine golide woyengeka m'moto, kuti ukakhale wachuma, ndi zovala zoyera, kuti ukadziveke, ndi kuti manyazi a usiwa wako asaoneke; ndi mankhwala opaka m'maso mwako, kuti ukaone.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa