Masalimo 119:172 - Buku Lopatulika172 Lilime langa liimbire mau anu; pakuti malamulo anu onse ndiwo olungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014172 Lilime langa liimbire mau anu; pakuti malamulo anu onse ndiwo olungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa172 Ndidzaimba nyimbo zoyamikira mau anu, chifukwa malamulo anu onse ndi olungama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero172 Lilime langa liyimbe mawu anu, popeza malamulo anu onse ndi olungama. Onani mutuwo |