Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:166 - Buku Lopatulika

166 Ndinayembekeza chipulumutso chanu, Yehova, ndipo ndinachita malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

166 Ndinayembekeza chipulumutso chanu, Yehova, ndipo ndinachita malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

166 Ndimakhulupirira kuti mudzandipulumutsa, Inu Chauta, ndipo ndimatsata malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

166 Ndikudikira chipulumutso chanu, Inu Yehova, ndipo ndimatsatira malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:166
10 Mawu Ofanana  

Ndadikira chipulumutso chanu, Yehova.


Ndinakhumba chipulumutso chanu, Yehova; ndipo chilamulo chanu ndicho chondikondweretsa.


Moyo wanga unakomoka ndi kukhumba chipulumutso chanu: Ndinayembekezera mau anu.


Iphani nsembe za chilungamo, ndipo mumkhulupirire Yehova.


Wopereka nsembe yachiyamiko andilemekeza Ine; ndipo kwa iye wosunga mayendedwe ake ndidzamuonetsa chipulumutso cha Mulungu.


Nkokoma kuti munthu ayembekeze ndi kulindirira modekha chipulumutso cha Yehova.


Ngati munthu aliyense afuna kuchita chifuniro chake, adzazindikira za chiphunzitsocho, ngati chichokera kwa Mulungu, kapena ndilankhula zochokera kwa Ine ndekha.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa