Masalimo 119:163 - Buku Lopatulika163 Ndidana nalo bodza ndi kunyansidwa nalo; koma ndikonda chilamulo chanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014163 Ndidana nalo bodza ndi kunyansidwa nalo; koma ndikonda chilamulo chanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa163 Ndimadana ndi anthu abodza, zoonadi, ndimanyansidwa nawo, koma ndimakonda malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero163 Ndimadana ndi chinyengo, kwambiri ndimanyansidwa nacho, koma ndimakonda malamulo anu. Onani mutuwo |