Masalimo 119:162 - Buku Lopatulika162 Ndikondwera nao mau anu, ngati munthu wakupeza zofunkha zambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014162 Ndikondwera nao mau anu, ngati munthu wakupeza zofunkha zambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa162 Ndimakondwa ndi mau anu monga munthu amene wapeza chuma chambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero162 Ine ndimakondwa ndi lonjezo lanu, ngati munthu amene wapeza chuma chambiri. Onani mutuwo |