Masalimo 119:16 - Buku Lopatulika16 Ndidzadzikondweretsa nao malemba anu; sindidzaiwala mau anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndidzadzikondweretsa nao malemba anu; sindidzaiwala mau anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndidzakondwera ndi malamulo anu, ndipo mau anu sindidzaŵaiŵala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndimakondwera ndi malamulo anu; sindidzayiwala konse mawu anu. Onani mutuwo |