Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:154 - Buku Lopatulika

154 Mundinenere mlandu wanga, nimundiombole; mundipatse moyo monga mwa mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

154 Mundinenere mlandu wanga, nimundiombole; mundipatse moyo monga mwa mau anu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

154 Munditchinjirize pa mlandu wanga, ndipo mundiwombole. Mundipatse moyo molingana ndi malonjezo anu aja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

154 Mundiyimirire pa mlandu wanga ndi kundiwombola; sungani moyo wanga molingana ndi lonjezo lanu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:154
15 Mawu Ofanana  

Koma ine ndikadafuna Mulungu, ndikadaikira mlandu wanga Mulungu;


Moyo wanga umamatika ndi fumbi; mundipatse moyo monga mwa mau anu.


Limbitsirani mtumiki wanu mau anu, ndiye wodzipereka kukuopani.


Taonani, ndinalira malangizo anu; mundipatse moyo mwa chilungamo chanu.


Tsutsanani nao iwo akutsutsana nane, Yehova; limbanani nao iwo akulimbana nane.


Galamukani, ndipo khalani maso kundiweruzira mlandu wanga, Mulungu wanga ndi Ambuye wanga.


Mundiweruzire, Mulungu, ndipo mundinenere mlandu kwa anthu opanda chifundo. Mundilanditse kwa munthu wonyenga ndi wosalungama.


Pakuti Yehova adzanenera mlandu wao; omwe akwatula zao Iye adzakwatula moyo wao.


Koma, Yehova wa makamu, amene aweruza molungama, amene ayesa impso ndi mtima, ndikuoneni Inu mulikuwabwezera chilango, pakuti kwa Inu ndawulula mlandu wanga.


Mombolo wao ngwa mphamvu; dzina lake Yehova wa makamu: adzawanenera mlandu wao ndithu; kuti apumutse dziko lapansi, nadzidzimutse okhala mu Babiloni.


Chifukwa chake Yehova atero: Taona, ndidzanenera iwe mlandu wako, ndidzawabwezera chilango chifukwa cha iwe; ndidzaphwetsa nyanja yake, ndidzaphwetsa chitsime chake.


Ndidzasenza mkwiyo wa Yehova, chifukwa ndamchimwira, mpaka andinenera mlandu wanga, ndi kundiweruzira mlandu wanga; adzanditulutsira kwa kuunika, ndipo ndidzapenya chilungamo chake.


Tiana tanga, izi ndikulemberani, kuti musachimwe. Ndipo akachimwa wina, Nkhoswe tili naye kwa Atate, ndiye Yesu Khristu wolungama;


Chifukwa chake Yehova akhale woweruza, naweruze pakati pa ine ndi inu, nayang'anire, nandigwirire moyo, nandipulumutse m'dzanja lanu.


Ndipo kunali, pakutsiriza Davide kulankhula mau awa kwa Saulo, Saulo anati, Ndiwo mau ako kodi, mwana wanga Davide? Saulo nakweza mau ake, nalira misozi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa