Masalimo 119:149 - Buku Lopatulika149 Imvani liu langa monga mwa chifundo chanu; mundipatse moyo monga mwa kuweruza kwanu, Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014149 Imvani liu langa monga mwa chifundo chanu; mundipatse moyo monga mwa kuweruza kwanu, Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa149 Imvani liwu langa chifukwa cha chikondi chanu chosasinthika. Inu Chauta, sungani moyo wanga chifukwa cha chilungamo chanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero149 Imvani mawu anga molingana ndi chikondi chanu chosasinthika; Yehova sungani moyo wanga, molingana ndi malamulo anu. Onani mutuwo |