Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 119:146 - Buku Lopatulika

146 Ndinaitanira Inu; ndipulumutseni, ndipo ndidzasamalira mboni zanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

146 Ndinaitanira Inu; ndipulumutseni, ndipo ndidzasamalira mboni zanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

146 Ndikukulirirani, mundipulumutse, kuti ndizitsata malamulo anu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

146 Ndikuyitana kwa Inu; pulumutseni ndipo ndidzasunga umboni wanu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 119:146
7 Mawu Ofanana  

Mundiombole kunsautso ya munthu: Ndipo ndidzasamalira malangizo anu.


Odala iwo akusunga mboni zake, akumfuna ndi mtima wonse;


Ine ndine wanu, ndipulumutseni pakuti ndinafuna malangizo anu.


Ndipo adzabala mwana wamwamuna, ndipo udzamutcha dzina lake Yesu; pakuti Iyeyo adzapulumutsa anthu ake kumachimo ao.


amene anadzipereka yekha m'malo mwa ife, kuti akatiombole ife kuzoipa zonse, nakadziyeretsere yekha anthu akhale ake enieni, achangu pa ntchito zokoma.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa