Masalimo 119:145 - Buku Lopatulika145 Ndinaitana ndi mtima wanga wonse; mundiyankhe, Yehova; ndidzasunga malemba anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014145 Ndinaitana ndi mtima wanga wonse; mundiyankhe, Yehova; ndidzasunga malemba anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa145 Ndikulira kwa Inu ndi mtima wanga wonse, mundiyankhe, Inu Chauta. Ndidzatsata malamulo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero145 Ndimayitana ndi mtima wanga wonse; ndiyankheni Inu Yehova, ndipo ndidzamvera zophunzitsa zanu. Onani mutuwo |