Masalimo 119:144 - Buku Lopatulika144 Mboni zanu ndizo zolungama kosatha; mundizindikiritse izi, ndipo ndidzakhala ndi moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 2014144 Mboni zanu ndizo zolungama kosatha; mundizindikiritse izi, ndipo ndidzakhala ndi moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa144 Malamulo anu ndi olungama mpaka muyaya, patseni nzeru zomvetsa kuti ndizikhala ndi moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero144 Umboni wanu ndi wabwino nthawi zonse; patseni nzeru zomvetsa zinthu kuti ine ndikhale ndi moyo. Onani mutuwo |