Masalimo 119:14 - Buku Lopatulika14 Ndinakondwera m'njira ya mboni zanu, koposa ndi chuma chonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndinakondwera m'njira ya mboni zanu, koposa ndi chuma chonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Kuyenda m'njira ya malamulo anu kumandikondwetsa, kupambana kukhala ndi chuma chilichonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndimakondwera potsatira malamulo anu monga momwe munthu amakondwera akakhala ndi chuma chambiri. Onani mutuwo |